Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Genesis 20:10 - Buku Lopatulika

10 Ndipo Abimeleki anati kwa Abrahamu, Unaona chiyani iwe kuti wachita ichi?

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

10 Ndipo Abimeleki anati kwa Abrahamu, Unaona chiyani iwe kuti wachita ichi?

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

10 Chifukwa chiyani wachita zimenezi?”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

10 Ndipo Abrahamu anafunsa Abimeleki kuti, “Chifukwa chiyani wachita zimenezi?”

Onani mutuwo Koperani




Genesis 20:10
3 Mawu Ofanana  

Ndipo Farao anaitana Abramu, nati, Nanga nchiyani ichi wandichitira ine? Chifukwa chanji sunandiuze ine kuti ndiye mkazi wako?


Ndipo Abrahamu anati, Chifukwa ndinati, Pompano palibe ndithu kumuopa Mulungu, ndipo adzandipha ine chifukwa cha mkazi wanga.


Ndipo Abimeleki anaitana Abrahamu, nati kwa iye, Watichitira ife chiyani iwe? Ndakuchimwiranji iwe kuti waufikitsa pa ine ndi pa ufumu wanga uchimo waukulu? Wandichitira ine zosayenera kuzichita.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa