Genesis 2:22 - Buku Lopatulika22 Ndipo nthitiyo anaichotsa Yehova Mulungu mwa Adamu anaipanga mkazi, ndipo ananka naye kwa Adamu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201422 Ndipo nthitiyo anaichotsa Yehova Mulungu mwa Adamu anaipanga mkazi, ndipo ananka naye kwa Adamu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa22 Chauta Mulungu adapanga mkazi ndi nthiti imene adaichotsa kwa Adamu uja, ndipo mkaziyo Mulungu adabwera naye kwa iye. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero22 Motero Yehova Mulungu anapanga mkazi ndi nthiti ija imene anatenga kwa munthu uja nabwera naye kwa iye. Onani mutuwo |