Genesis 17:11 - Buku Lopatulika11 Muzidula khungu lanu; ndipo chidzakhala chizindikiro cha pangano pakati pa Ine ndi inu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201411 Muzidula khungu lanu; ndipo chidzakhala chizindikiro cha pangano pakati pa Ine ndi inu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa11 Kuyambira tsopano muziwumbalidwa. Chimenechi chidzakhala chizindikiro cha chipangano pakati pa Ine ndi inu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero11 Kuyambira tsopano muzichita mdulidwe ndipo ichi chidzakhala chizindikiro cha pangano langa ndi iwe. Onani mutuwo |