Genesis 14:21 - Buku Lopatulika21 Mfumu ya Sodomu ndipo inati kwa Abramu, Ndipatse ine anthu, nutenge chuma iwe wekha. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201421 Mfumu ya Sodomu ndipo inati kwa Abramu, Ndipatse ine anthu, nutenge chuma iwe wekha. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa21 Komanso mfumu ya ku Sodomu idapempha Abramu kuti “Zinthu zonse mudatengazi, musunge, koma anthu anga okhaŵa mundipatse.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero21 Mfumu ya Sodomu inati kwa Abramu, “Ine undipatse anthu okhawo, koma katundu akhale wako.” Onani mutuwo |