Genesis 14:19 - Buku Lopatulika19 Ndipo anamdalitsa iye, nati, Abramu adalitsike ndi Mulungu Wamkulukulu, mlengi wa kumwamba ndi dziko lapansi; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201419 Ndipo anamdalitsa iye, nati, Abramu adalitsike ndi Mulungu Wamkulukulu, mwini kumwamba ndi dziko lapansi; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa19 Adadalitsa Abramuyo, adati, “Mulungu Wopambanazonse, Mlengi wa kumwamba ndi dziko lapansi, akudalitse iwe Abramu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero19 ndipo anadalitsa Abramu nati, “Mulungu Wammwambamwamba, wolenga kumwamba ndi dziko lapansi, akudalitse iwe Abramu. Onani mutuwo |