Genesis 14:16 - Buku Lopatulika16 Ndipo anabwera nacho chuma chonse, nabwera naye Loti yemwe ndi chuma chake, ndi akazi ndi anthu omwe. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201416 Ndipo anabwera nacho chuma chonse, nabwera naye Loti yemwe ndi chuma chake, ndi akazi ndi anthu omwe. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa16 ndipo adaŵalanda zao zonse. Adabwera naye Loti, mwana wa mbale wake, pamodzi ndi zake zonse, kuphatikizapo akazi ndi anthu ena onse. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero16 Ndipo anawalanda katundu wawo yense nabwera naye Loti, katundu wake yense, pamodzi ndi akazi ndi anthu ena. Onani mutuwo |