Genesis 13:9 - Buku Lopatulika9 Dziko lonse silili pamaso pako kodi? Ulekanetu ndi ine: ukanka iwe ku dzanja lamanzere, ine ndinka ku dzanja lamanja: ukanka iwe ku dzanja lamanja, ine ndinka ku dzanja lamanzere. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 Dziko lonse silili pamaso pako kodi? Ulekanetu ndi ine: ukanka iwe ku dzanja lamanzere, ine ndinka ku dzanja lamanja: ukanka iwe ku dzanja lamanja, ine ndinka ku dzanja lamanzere. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 Tiye tisiyane, usankhe dera lina lililonse la dziko lino limene ufuna. Iwe ukapita kwina, inenso ndipita kwina.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 Kodi dziko lonseli silili pamaso pako? Tiye tisiyane. Iwe ukalowera kumanzere, ine ndilowera kumanja; ukalowera kumanja, ine ndipita kumanzere.” Onani mutuwo |