Genesis 13:15 - Buku Lopatulika15 chifukwa kuti dziko lonse limene ulinkuona, ndidzakupatsa iwe ndi mbeu yako nthawi yonse. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201415 chifukwa kuti dziko lonse limene ulinkuona, ndidzakupatsa iwe ndi mbeu yako nthawi yonse. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa15 Ndidzakupatsa dziko lonse limene ukuliwonalo, iweyo pamodzi ndi zidzukulu zako. Ndipo lidzakhala lako mpaka muyaya. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero15 Dziko lonse ukulionalo ndidzalipereka kwa iwe ndi zidzukulu zako mpaka muyaya. Onani mutuwo |