Genesis 13:11 - Buku Lopatulika11 Ndipo Loti anasankha chigwa chonse cha Yordani; ndipo Loti anachoka ulendo wake kunka kum'mawa: ndipo analekana wina ndi mnzake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201411 Ndipo Loti anasankha chigwa chonse cha Yordani; ndipo Loti anachoka ulendo wake kunka kum'mawa: ndipo analekana wina ndi mnzake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa11 Loti adadzisankhira chigwa chonse cha Yordani, napita kukakhala chakuvuma. Umu ndimo m'mene anthu aŵiriwo adasiyanirana. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero11 Choncho Loti anadzisankhira yekha chigwa chonse cha Yorodani nanyamuka kulowera cha kummawa. Choncho anthu awiriwa anasiyana. Onani mutuwo |