Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Genesis 12:9 - Buku Lopatulika

9 Ndipo Abramu anayenda ulendo wake, nayendayenda kunka kumwera.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

9 Ndipo Abramu anayenda ulendo wake, nayendayenda kunka kumwera.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

9 Adapitirira ulendo wake pang'onopang'ono, kuloŵera ku Negebu, chigawo chakumwera.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

9 Kenaka Abramu ananyamuka kumalowera cha ku Negevi.

Onani mutuwo Koperani




Genesis 12:9
10 Mawu Ofanana  

Ndipo anakwera Abramu kuchoka ku Ejipito, iye ndi mkazi wake, ndi zonse anali nazo, ndi Loti pamodzi naye, kunka ku dziko la kumwera.


Ndipo anankabe ulendo wake kuchokera ku dziko la kumwera kunka ku Betele, kufikira kumalo kumene kunali hema wake poyamba paja pakati pa Betele ndi Ai;


Abrahamu ndipo anachoka kumeneko kunka ku dziko la kumwera, ndipo anakhala pakati pa Kadesi ndi Suri, ndipo anakhala ngati mlendo mu Gerari.


Ndipo panali pamene Mulungu anandiyendetsa ine kunyumba kwa atate wanga, ndinati kwa mkaziyo, Ichi ndicho chokoma mtima udzandichitire ine, konse kumene tidzafika ife, uzinena za ine, Iye ndiye mlongo wanga.


Ndipo Isaki anadzera njira ya Beere-Lahai-Roi; chifukwa kuti anakhala iye m'dziko la kumwera.


nayendayenda kuchokera mtundu wina kufikira mtundu wina, kuchokera ufumu wina kufikira anthu ena.


Katundu wa zilombo za kumwera. M'dziko lovuta ndi lopweteka, kumeneko kuchokera mkango waukazi, ndi wamphongo, mphiri, ndi njoka youluka yamoto, iwo anyamula chuma chao pamsana pa abulu, ndi ang'ono zolemera zao pa malinundu a ngamira, kunka kwa anthu amene sadzapindula nao.


Potero Mose anawatuma azonde dziko la Kanani, nanena nao, Kwerani uko kumwera, nimukwere kumapiri;


bwererani, yendani ulendo wanu ndi kumuka ku mapiri a Aamori, ndi koyandikizana nao, kuchidikha, kumapiri, ndi kunsi ndi kumwera, ndi kumphepete kwa nyanja, dziko la Akanani, ndi Lebanoni, kufikira mtsinje waukulu wa Yufurate.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa