Genesis 12:9 - Buku Lopatulika9 Ndipo Abramu anayenda ulendo wake, nayendayenda kunka kumwera. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 Ndipo Abramu anayenda ulendo wake, nayendayenda kunka kumwera. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 Adapitirira ulendo wake pang'onopang'ono, kuloŵera ku Negebu, chigawo chakumwera. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 Kenaka Abramu ananyamuka kumalowera cha ku Negevi. Onani mutuwo |