Genesis 12:20 - Buku Lopatulika20 Ndipo Farao analamulira anthu ake za iye; ndipo anamperekeza iye m'njira ndi mkazi wake ndi zonse anali nazo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201420 Ndipo Farao analamulira anthu ake za iye; ndipo anamperekeza iye m'njira ndi mkazi wake ndi zonse anali nazo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa20 Farao adalamula anthu ake, ndipo iwowo adatulutsa Abramu ndi mkazi wake m'dzikomo, pamodzi ndi zonse zimene anali nazo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero20 Farao analamula asilikali ake ndipo iwo anamutulutsa Abramu pamodzi ndi mkazi wake ndi zonse anali nazo. Onani mutuwo |