Genesis 12:17 - Buku Lopatulika17 Koma Yehova anavutitsa Farao ndi banja lake ndi nthenda zazikulu chifukwa cha Sarai mkazi wake wa Abramu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201417 Koma Yehova anavutitsa Farao ndi banja lake ndi nthenda zazikulu chifukwa cha Sarai mkazi wake wa Abramu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa17 Koma Chauta adagwetsa nthenda zoopsa pa Farao ndi pa anthu a m'nyumba mwake omwe, chifukwa cha Sarai mkazi wa Abramu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero17 Koma Yehova anabweretsa matenda owopsa pa Farao pamodzi ndi banja lake lonse chifukwa cha Sarai mkazi wa Abramu. Onani mutuwo |