Genesis 12:14 - Buku Lopatulika14 Ndipo panali pamene Abramu analowa mu Ejipito, Aejipito anaona kuti mkazi anali wokongola kwambiri. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201414 Ndipo panali pamene Abramu analowa m'Ejipito, Aejipito anaona kuti mkazi anali wokongola kwambiri. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa14 Abramu ataoloka malire kuloŵa mu Ejipito, Aejipito adaonadi kuti mkazi wake ndi wokongola kwambiri. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero14 Pamene Abramu anafika ku Igupto, Aigupto aja anaona kuti Sarai anali mkazi wokongoladi. Onani mutuwo |