Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Genesis 11:30 - Buku Lopatulika

30 Koma Sarai anali wouma; analibe mwana.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

30 Koma Sarai anali wouma; analibe mwana.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

30 Sarai analibe ana chifukwa anali wosabala.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

30 Sarai analibe ana chifukwa anali wosabereka.

Onani mutuwo Koperani




Genesis 11:30
14 Mawu Ofanana  

Ndipo Tera anatenga Abramu mwana wake wamwamuna, ndi Loti mwana wa Harani, mwana wake wamwamuna, ndi Sarai mpongozi wake, mkazi wa mwana wake Abramu; ndipo anatuluka pamodzi nao ku Uri wa kwa Akaldeya kuti amuke ku dziko la Kanani, ndipo anafika ku Harani, nakhala kumeneko.


Ndipo Isaki anampembedzera mkazi wake kwa Yehova popeza anali wouma: ndipo Yehova analola kupembedza kwake, ndipo Rebeka mkazi wake anatenga pakati.


Pamene Yehova anaona kuti anamuda Leya, anatsegula m'mimba mwake; koma Rakele anali wouma.


Asungitsa nyumba mkazi wosaona mwana, akhale mai wokondwera ndi ana. Aleluya.


Ndipo taona, Elizabeti mbale wako, iyenso ali ndi pakati pa mwana wamwamuna mu ukalamba wake; ndipo mwezi uno uli wachisanu ndi chimodzi wa iye amene ananenedwa wouma.


Ndipo analibe mwana, popeza Elizabeti anali wouma, ndipo onse awiri anakalamba.


Ndipo panali munthu wina wa Zora wa banja la Adani, dzina lake ndiye Manowa; ndi mkazi wake analibe mwana, sanabale.


Iyeyu anali nao akazi awiri; winayo dzina lake ndi Hana, mnzake dzina lake ndi Penina. Ndipo Penina anaona ana, koma Hana anali wouma.


koma anapatsa Hana magawo awiri, chifukwa anakonda Hana, koma Yehova anatseka mimba yake.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa