Genesis 11:28 - Buku Lopatulika28 Ndipo anafa Harani pamaso pa atate wake Tera m'dziko la kubadwa kwake, mu Uri wa kwa Akaldeya. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201428 Ndipo anafa Harani pamaso pa atate wake Tera m'dziko la kubadwa kwake, m'Uri wa kwa Akaldeya. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa28 Haraniyo adafera m'mudzi wa kwao dzina lake Uri, wa ku Kaldeya. Adafa atate ake akali moyo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero28 Abambo ake a Tera akanali ndi moyo, Harani anamwalira ku Uri wa ku Akaldeya kumene anabadwira. Onani mutuwo |