Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Genesis 11:10 - Buku Lopatulika

10 Mibadwo ya Semu ndi iyi: Semu anali wa zaka zana limodzi ndipo anabala Aripakisadi, chitapita chigumula zaka ziwiri;

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

10 Mibadwo ya Semu ndi iyi: Semu anali wa zaka zana limodzi ndipo anabala Aripakisadi, chitapita chigumula zaka ziwiri;

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

10 Nayi mibadwo yofumira mwa Semu: Patangopita zaka ziŵiri chitatha chigumula, Semu ali wa zaka 100, adabereka mwana dzina lake Aripakisadi.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

10 Nayi mibado yochokera kwa Semu. Patapita zaka ziwiri chitatha chigumula, Semu ali ndi zaka 100, anabereka Aripakisadi.

Onani mutuwo Koperani




Genesis 11:10
5 Mawu Ofanana  

ndipo Semu anakhala ndi moyo zaka mazana asanu, atabala Aripakisadi, nabala ana aamuna ndi aakazi.


Mibadwo ya Tera ndi iyi: Tera anabala Abramu, ndi Nahori, ndi Harani; ndipo Harani anabala Loti.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa