Eksodo 9:28 - Buku Lopatulika28 Pembani kwa Yehova; chifukwa akwanira ndithu mabingu a Mulungu ndi matalala; ndipo ndidzakulolani mumuke, osakhalanso. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201428 Pembani kwa Yehova; chifukwa akwanira ndithu mabingu a Mulungu ndi matalala; ndipo ndidzakulolani mumuke, osakhalanso. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa28 Pemphera kwa Chauta kuti aŵaletse mabingu ndi matalalaŵa ndipo ndidzakulolani kuti mupite. Simudzakhalanso kuno ai.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero28 Upemphere kwa Mulungu chifukwa mabingu ndi matalala atikwana. Ine ndidzakulolani kuti mupite. Simuyenera kukhalabe kuno.” Onani mutuwo |