Eksodo 8:27 - Buku Lopatulika27 Timuke ulendo wa masiku atatu m'chipululu, tikamphere Yehova Mulungu wathu nsembe, monga adzanena nafe. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201427 Timuke ulendo wa masiku atatu m'chipululu, tikamphere Yehova Mulungu wathu nsembe, monga adzanena nafe. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa27 Tiyenera kuyenda ulendo wa masiku atatu m'chipululu, kuti tikapereke nsembe kwa Chauta, Mulungu wathu, monga adatilamulira.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero27 Ife tiyenera kuyenda ulendo wa masiku atatu kupita ku chipululu kukapereka nsembe kwa Yehova Mulungu wathu monga anatilamulira.” Onani mutuwo |