Eksodo 8:13 - Buku Lopatulika13 Ndipo Yehova anachita monga mwa mau a Mose; nafa achulewo kuchokera m'zinyumba, ndi m'mabwalo, ndi m'minda. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201413 Ndipo Yehova anachita monga mwa mau a Mose; nafa achulewo kuchokera m'zinyumba, ndi m'mabwalo, ndi m'minda. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa13 Tsono Chauta adachitadi monga momwe Mose adapemphera. Motero achule onse aja amene adaali m'nyumba, pa bwalo ndi m'minda momwe, adafa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero13 Ndipo Yehova anachita zomwe Mose anapempha. Achule amene anali mʼnyumba, mʼmabwalo ndi mʼminda anafa Onani mutuwo |