Eksodo 40:24 - Buku Lopatulika24 Ndipo anaika choikaponyali m'chihema chokomanako, popenyana ndi gome, pa mbali ya kumwera ya Kachisi. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201424 Ndipo anaika choikapo nyali m'chihema chokomanako, popenyana ndi gome, pa mbali ya kumwera ya Kachisi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa24 M'chihema chamsonkanomo adaikamo choikaponyale mopenyana ndi tebulo chakumwera kwake kwa malo opatulika. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero24 Iye anayikanso choyikapo nyale mu tenti ya msonkhano moyangʼanana ndi tebulo mbali yakummwera kwa chihema. Onani mutuwo |