Eksodo 39:2 - Buku Lopatulika2 Ndipo anaomba efodi wa golide, lamadzi, lofiirira, ndi lofiira, ndi bafuta wa thonje losansitsa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Ndipo anaomba efodi wa golide, lamadzi, lofiirira, ndi lofiira, ndi bafuta wa thonje losansitsa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Adapanga chovala chopatulika cha efodi ndi nsalu yagolide ndiponso ndi nsalu yobiriŵira, yofiirira ndi yofiira, ndi ya bafuta wosalala ndi wopikidwa bwino. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Popanga efodi, iwo anagwiritsa ntchito golide, nsalu yamtundu wa mtambo, yapepo, yofiira, yosalala yofewa. Onani mutuwo |