Eksodo 39:17 - Buku Lopatulika17 Ndipo anamanga maunyolo awiri opota agolide pa mphete ziwiri pansonga za chapachifuwa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201417 Ndipo anamanga maunyolo awiri opota agolide pa mphete ziwiri pa nsonga za chapachifuwa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa17 Tsono zingwe ziŵiri zagolide adazilumikiza ku mphete ziŵiri zija, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero17 Anamangirira timaunyolo tiwiri tagolide tija pa mphete za pa ngodya pa chovala chapachifuwacho. Onani mutuwo |