Eksodo 39:15 - Buku Lopatulika15 Ndipo anapangira pachapachifuwa maunyolo ngati zingwe, ntchito yopota ya golide woona. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201415 Ndipo anapangira pachapachifuwa maunyolo ngati zingwe, ntchito yopota ya golide woona. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa15 Adapanga timaunyolo ta chovala chapachifuwa ta golide wabwino kwambiri, topota mwaluso ngati maukufu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero15 Anapanga timaunyolo tagolide wabwino kwambiri ta pa chovala chapachifuwa, topota ngati chingwe. Onani mutuwo |