Eksodo 38:10 - Buku Lopatulika10 nsichi zake makumi awiri, ndi makamwa ao makumi awiri, amkuwa; zokowera za nsichi ndi mitanda yake zasiliva. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201410 nsichi zake makumi awiri, ndi makamwa ao makumi awiri, amkuwa; zokowera za nsichi ndi mitanda yake zasiliva. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa10 Nsanamira zake makumi aŵiri, pamodzi ndi masinde ake makumi aŵiri, zonsezo zinali zamkuŵa, koma ngoŵe za pa nsanamirazo, pamodzi ndi mitanda yake, zinali zasiliva. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero10 Anapanganso mizati makumi awiri, matsinde makumi awiri amkuwa ndi ngowe zasiliva ndi zingwe za mizatiyo. Onani mutuwo |