Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Eksodo 36:6 - Buku Lopatulika

6 Ndipo Mose analamulira, ndipo anamveketsa mau mu chigono chonse, ndi kuti, Asaonjezere ntchito ya ku chopereka cha malo opatulika, ngakhale mwamuna ngakhale mkazi. Tero anawaletsa anthu asabwere nazo zina.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

6 Ndipo Mose analamulira, ndipo anamveketsa mau mwa chigono chonse, ndi kuti, Asaonjezere ntchito ya ku chopereka cha malo opatulika, ngakhale mwamuna ngakhale mkazi. Tero anawaletsa anthu asabwere nazo zina.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

6 Motero Mose adalamula anthu m'mahema monse kuti, “Mwamuna aliyense ndi mkazi aliyense asaperekenso zopereka zomangira malo opatulika.” Motero anthu adaleka kubwera ndi zopereka.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

6 Choncho Mose analamulira ndipo analengeza mu msasa onse, “Mwamuna kapena mayi aliyense asaperekenso chopereka chilichonse cha ku malo wopatulika.” Choncho anthu analetsedwa kubweretsa zambiri,

Onani mutuwo Koperani




Eksodo 36:6
2 Mawu Ofanana  

nanena ndi Mose, ndi kuti, Anthu alinkubwera nazo zochuluka, zakuposera zoyenera ntchito imene Yehova analamula ichitike.


Popeza zipangizo zinakwanira ntchito yonse ichitike, zinatsalakonso.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa