Eksodo 32:28 - Buku Lopatulika28 Ndipo ana a Levi anachita monga mwa mau a Mose; ndipo adagwa tsiku lija anthu ngati zikwi zitatu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201428 Ndipo ana a Levi anachita monga mwa mau a Mose; ndipo adagwa tsiku lija anthu ngati zikwi zitatu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa28 Aleviwo adachitadi monga momwe Mose adaŵalamulira, ndipo amuna 3,000 adaphedwa pa tsiku limenelo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero28 Alevi anachita zomwe Mose analamula, ndipo tsiku limenelo panafa anthu pafupifupi 3,000. Onani mutuwo |