Eksodo 32:22 - Buku Lopatulika22 Ndipo Aroni anati, Asapse mtima mbuye wanga; udziwa anthuwa kuti akhumba choipa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201422 Ndipo Aroni anati, Asapse mtima mbuye wanga; udziwa anthuwa kuti akhumba choipa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa22 Aroni adayankha kuti, “Musakwiyire ine mbuyanga. Mumaŵadziŵa anthu ameneŵa kuti ngovuta. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero22 Aaroni anayankha kuti, “Musakwiye mbuye wanga. Inu mukudziwa kuti anthu awa ndi ovuta. Onani mutuwo |