Eksodo 31:2 - Buku Lopatulika2 Taona ndaitana ndi kumtchula dzina lake, Bezalele, mwana wa Uri, mwana wa Huri, wa fuko la Yuda; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Taona ndaitana ndi kumtchula dzina lake, Bezalele, mwana wa Uri, mwana wa Huri, wa fuko la Yuda; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 “Ndasankha Bezalele mwana wa Uri, mdzukulu wa Huri, wa fuko la Yuda. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 “Taona, ndasankha Bezaleli mwana wa Uri, mwana wa Huri, wa fuko la Yuda. Onani mutuwo |