Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Eksodo 29:6 - Buku Lopatulika

6 ndipo uike nduwira pamutu pake, ndi kuika korona wopatulika panduwirapo.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

6 ndipo uike nduwira pamutu pake, ndi kuika korona wopatulika panduwirapo.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

6 Umuveke nduŵira kumutu kwake, ndi duŵa lopatulika lija panduŵirapo.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

6 Umuveke nduwira kumutu, ndiponso uyike chizindikiro chopatulika chija pa nduwirayo.

Onani mutuwo Koperani




Eksodo 29:6
5 Mawu Ofanana  

Ndipo zovala azisoka ndi izi: chapachifuwa ndi efodi, ndi mwinjiro, ndi malaya opikapika, ndi nduwira, ndi mpango; tero apangire Aroni mbale wako ndi ana ake zovala zopatulika, kuti andichitire Ine ntchito ya nsembe.


Asatuluke m'malo opatulika, kapena kuipsa malo opatulika a Mulungu wake; popeza korona wa mafuta odzoza wa Mulungu wake ali pa iye; Ine ndine Yehova.


Naika nduwirayo pamutu pake; ndi panduwira, pamphumi pake anaika golide waphanthiphanthi, ndiwo korona wopatulika; monga Yehova adauza Mose.


Ndipo ndinati, Amuike nduwira yoyera pamutu pake. Naika nduwira yoyera pamutu pake, namveka ndi zovala; ndi mthenga wa Yehova anaimirirapo.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa