Eksodo 29:13 - Buku Lopatulika13 Nutenge mafuta onse akukuta matumbo, ndi chokuta cha mphafa ndi impso ziwiri, ndi mafuta ali pa izo, ndi kuzitentha paguwa la nsembe. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201413 Nutenge mafuta onse akukuta matumbo, ndi chokuta cha mphafa ndi impso ziwiri, ndi mafuta ali pa izo, ndi kuzitentha pa guwa la nsembe. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa13 Pambuyo pake utenge mafuta onse okuta matumbo, mphumphu ya mafuta akuchiŵindi, ndiponso imso ziŵiri, pamodzi ndi mafuta ozikuta. Zonsezi uzipereke, ndipo uzitenthere pa guwalo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero13 Kenaka utenge mafuta onse okuta matumbo, mafuta ophimba chiwindi ndiponso impsyo zonse ziwiri pamodzi ndi mafuta ake. Zonsezi uzitenthe pa guwapo. Onani mutuwo |