Eksodo 23:33 - Buku Lopatulika33 Asakhale m'dziko lako iwowa, kuti angakulakwitse pa Ine; pakuti ukatumikira milungu yao, kudzakukhalira msampha ndithu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201433 Asakhale m'dziko lako iwowa, kuti angakulakwitse pa Ine; pakuti ukatumikira milungu yao, kudzakukhalira msampha ndithu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa33 Asadzakhale m'dziko mwanu, kuwopa kuti angadzakuchimwitseni. Mukamapembedza milungu yao, ndithu mudzakodwa mu msampha.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero33 Asadzakhale mʼdziko lanu chifukwa angadzakuchimwitseni ndi kuyamba kupembedza milungu yawo. Mukadzatero ndiye kuti mwakodwa mu msampha.” Onani mutuwo |