Eksodo 22:23 - Buku Lopatulika23 Ukawazunza ndi kakuti konse, nakandilirira pang'ono ponse iwowa, ndidzamvadi kulira kwao; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201423 Ukawazunza ndi kakuti konse, nakandilirira pang'ono ponse iwowa, ndidzamvadi kulira kwao; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa23 Mukamaŵazunza, Ine ndidzaŵamva iwowo akamalira kwa Ine. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero23 Ngati muwazunza ndipo iwo nʼkulirira kwa Ine, ndidzamva kulira kwawo. Onani mutuwo |