Eksodo 20:6 - Buku Lopatulika6 ndi kuwachitira chifundo anthu zikwizikwi a iwo amene akondana ndi Ine, nasunga malamulo anga. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 ndi kuwachitira chifundo anthu zikwizikwi a iwo amene akondana ndi Ine, nasunga malamulo anga. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 Komatu anthu ambirimbiri a mibadwo yosaŵerengeka amene amandikonda, namatsata malamulo anga, ndimaŵakonda ndi chikondi chosasinthika. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 Koma ndimaonetsa chikondi chosasinthika ku mibado miyandamiyanda ya anthu amene amandikonda, ndi kusunga malamulo anga. Onani mutuwo |