Eksodo 20:2 - Buku Lopatulika2 Ine ndine Yehova Mulungu wako, amene ndinatulutsa iwe ku dziko la Ejipito, kunyumba ya ukapolo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Ine ndine Yehova Mulungu wako, amene ndinatulutsa iwe ku dziko la Ejipito, kunyumba ya akapolo Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 “Ine ndine Chauta Mulungu wako, amene ndidakutulutsa mu ukapolo ku dziko la Ejipito. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 “Ine ndine Yehova Mulungu wako amene ndinakutulutsa ku Igupto, mʼdziko la ukapolo. Onani mutuwo |