Eksodo 20:19 - Buku Lopatulika19 Ndipo anati kwa Mose, Mulankhule nafe ndinu, ndipo tidzamva; koma asalankhule nafe Mulungu, kuti tingafe. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201419 Ndipo anati kwa Mose, Mulankhule nafe ndinu, ndipo tidzamva; koma asalankhule nafe Mulungu, kuti tingafe. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa19 Adauza Mose kuti, “Muzilankhula ndi ife ndinu, ndipo tidzamva. Mulungu asalankhule nafe, kuti tingafe.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero19 Ndipo anati kwa Mose, “Iwe utiyankhule ndipo tidzamvera. Koma usalole kuti Mulungu atiyankhule, tingafe.” Onani mutuwo |