Eksodo 2:24 - Buku Lopatulika24 Ndipo Mulungu anamva kubuula kwao, ndi Mulungu anakumbukira chipangano chake ndi Abrahamu, ndi Isaki, ndi Yakobo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201424 Ndipo Mulungu anamva kubuula kwao, ndi Mulungu anakumbukira chipangano chake ndi Abrahamu, ndi Isaki, ndi Yakobo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa24 Mulungu adamva kudandaula kwaoko, nakumbukira chipangano chake chija chimene adachita ndi Abrahamu, Isaki ndi Yakobe. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero24 Mulungu anamva kubuwula kwawo ndipo anakumbukira pangano lake ndi Abrahamu, Isake ndi Yakobo. Onani mutuwo |