Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Eksodo 18:24 - Buku Lopatulika

24 Ndipo Mose anamvera mau a mpongozi wake, nachita zonse adazinena.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

24 Ndipo Mose anamvera mau a mpongozi wake, nachita zonse adazinena.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

24 Mose adamvera zonse zimene adanena Yetero zija.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

24 Mose anamvera mpongozi wake ndi kuchita zonse zimene iye ananena.

Onani mutuwo Koperani




Eksodo 18:24
10 Mawu Ofanana  

Pamenepo Sekaniya mwana wa Yehiyele, mwana wina wa Elamu, anambwezera Ezara mau, nati, Talakwira Mulungu wathu, tadzitengera akazi achilendo a mitundu ya dzikoli; koma tsopano chimtsalira Israele chiyembekezo kunena za chinthu ichi.


Nanyamuka Ezara, nalumbiritsa akulu a ansembe, ndi Alevi, ndi Aisraele onse, kuti adzachita monga mwa mau awa. Nalumbira iwo.


Ndipo anawatsogolera mokhulupirika, kotero kuti sanaope; koma nyanja inamiza adani ao.


Tamvera mau anga tsopano, ndikupangire nzeru, ndi Mulungu akhale nawe; ukhale m'malo mwa anthu kwa Mulungu, nupite nayo milandu kwa Mulungu;


Ukachite chinthuchi, ndi Mulungu akakuuza chotero, udzakhoza kupirira, ndi anthu awa onse adzapita kwao mumtendere.


Ndipo Mose anasankha amuna anzeru mwa Aisraele onse, nawaika akulu a pa anthu, akulu a pa zikwi, akulu a pa mazana, akulu a pa makumi asanu, ndi akulu a pa makumi.


kuti wanzeru amve, naonjezere kuphunzira; ndi kuti wozindikira afikire kuuphungu;


Ndipo diso silingathe kunena kwa dzanja, Sindikufuna iwe, kapenanso mutu kwa mapazi, Sindikufunani inu.


Ndipo muja ndinanena ndi inu, ndi kuti, Sinditha ine kukunyamulani ndekha;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa