Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Eksodo 16:30 - Buku Lopatulika

30 Ndipo anthu anapumula tsiku lachisanu ndi chiwiri.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

30 Ndipo anthu anapumula tsiku lachisanu ndi chiwiri.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

30 Motero anthu sankagwira ntchito pa tsiku lachisanu ndi chiŵiri.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

30 Kotero anthu anapuma tsiku lachisanu ndi chiwiri.

Onani mutuwo Koperani




Eksodo 16:30
5 Mawu Ofanana  

Taonani, popeza Yehova anakupatsani Sabata, chifukwa chake tsiku lachisanu ndi chimodzi alikupatsa inu mkate wofikira masiku awiri; khalani yense m'malo mwake munthu asatuluke m'malo mwake tsiku lachisanu ndi chiwiri.


Ndipo mbumba ya Israele inautcha dzina lake Mana; ndiwo ngati zipatso zampasa, oyera; powalawa akunga timitanda tosakaniza ndi uchi.


Masiku asanu ndi limodzi azigwira ntchito; koma lachisanu ndi chiwiri ndilo Sabata lakupumula, msonkhano wopatulika; musamagwira ntchito konse; ndilo Sabata la Yehova m'nyumba zanu zonse.


Momwemo utsalira mpumulo wa Sabata wa kwa anthu a Mulungu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa