Eksodo 15:21 - Buku Lopatulika21 Ndipo Miriyamu anawayankha, Imbirani Yehova, pakuti wapambanatu; kavalo ndi wokwera wake anawaponya m'nyanja. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201421 Ndipo Miriyamu anawayankha, Imbirani Yehova, pakuti wapambanatu; kavalo ndi wokwera wake anawaponya m'nyanja. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa21 Ndipo Miriyamu adaŵaimbira iwowo nyimbo yakuti, “Imbirani Chauta chifukwa wapambana, waponya m'nyanja akavalo pamodzi ndi okwerapo ake omwe.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero21 Miriamu anawayimbira nyimbo iyi: “Imbirani Yehova, chifukwa iye wapambana. Kavalo ndi wokwerapo wake Iye wawamiza mʼnyanja.” Onani mutuwo |
Ndipo kunali, pakuchita limodzi amalipenga ndi oimba, kumveketsa mau amodzi akulemekeza ndi kuyamika Yehova, ndi pakukweza mau ao pamodzi ndi malipenga, ndi nsanje, ndi zoimbira zina, ndi kulemekeza Yehova, ndi kuti, Pakuti Iye ndiye wabwino, pakuti chifundo chake chikhala chikhalire; pamenepo mtambo unadzaza nyumbayi, ndiyo nyumba ya Yehova;