Eksodo 14:26 - Buku Lopatulika26 Ndipo Yehova anati kwa Mose, Tambasulira dzanja lako kunyanja, kuti madziwo abwerere kudzamiza Aejipito, magaleta ao, ndi apakavalo ao. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201426 Ndipo Yehova anati kwa Mose, Tambasulira dzanja lako kunyanja, kuti madziwo abwerere kudzamiza Aejipito, magaleta ao, ndi apakavalo ao. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa26 Apo Chauta adauza Mose kuti, “Tambalitsa dzanja lako kunyanjako kuti madziwo abwerere, ndi kumiza Aejipitowo pamodzi ndi magaleta ao ndi oŵayendetsa ake omwe.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero26 Kenaka Yehova anati kwa Mose, “Tambasula dzanja lako pa nyanja kuti madzi amize Aigupto ndi magaleta awo ndi okwera pa akavalo.” Onani mutuwo |