Eksodo 14:18 - Buku Lopatulika18 Ndipo Aejipito adzadziwa kuti Ine ndine Yehova, polemekezedwa Ine pa Farao, pa magaleta ake, ndi pa okwera pa akavalo ake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201418 Ndipo Aejipito adzadziwa kuti Ine ndine Yehova, polemekezedwa Ine pa Farao, pa magaleta ake, ndi pa okwera pa akavalo ake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa18 Aejipitowo adzadziŵa kuti Ine ndine Chauta, akadzaona m'mene ndipambanire Farao ndi magaleta ake ndi oŵayendetsa ake.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero18 Aigupto adzadziwa kuti Ine ndine Yehova akadzaona mmene ndipambanire Farao ndi magaleta ndi owayendetsa ake.” Onani mutuwo |