Eksodo 13:11 - Buku Lopatulika11 Ndipo kudzakhala, atakulowetsa Yehova m'dziko la Akanani, monga anakulumbirira iwe ndi makolo ako, ndipo anakupatsa ilo, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201411 Ndipo kudzakhala, atakulowetsa Yehova m'dziko la Akanani, monga anakulumbirira iwe ndi makolo ako, ndipo anakupatsa ilo, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa11 “Chauta adzakuloŵetsani m'dziko la Akanani limene adakulonjezani pamodzi ndi makolo anu. Akadzakupatsani dziko, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero11 “Yehova akadzakulowetsani ndi kukupatsani dziko la Kanaani monga analonjezera kwa inu ndi makolo anu, Onani mutuwo |