Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Eksodo 12:20 - Buku Lopatulika

20 Musadye kanthu ka chotupitsa; mokhala inu monse muzidya mkate wopanda chotupitsa.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

20 Musadye kanthu ka chotupitsa; mokhala inu monse muzidya mkate wopanda chotupitsa.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

20 Musadye chilichonse chofufumitsa, ndipo ku nyumba zanu zonse muzidzangodya buledi wosafufumitsa.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

20 Musadye chilichonse chokhala ndi yisiti. Kulikonse kumene mukukhala, muyenera kudya buledi wopanda yisiti.”

Onani mutuwo Koperani




Eksodo 12:20
4 Mawu Ofanana  

Chisapezeke chotupitsa m'nyumba zanu masiku asanu ndi awiri; pakuti aliyense wakudya kanthu ka chotupitsa, munthuyo adzachotsedwa ku gulu la Israele, angakhale ndiye mlendo kapena wobadwa m'dziko.


Pamenepo Mose anaitana akulu onse a Israele, nanena nao, Pitani, dzitengereni anaankhosa monga mwa mabanja anu, nimuphere Paska.


Usapereke mwazi wa nsembe yanga yophera pamodzi ndi mkate wachotupitsa; ndi nsembe yophera ya chikondwerero cha Paska asaisiye kufikira m'mawa.


Fanizo lina ananena kwa iwo; Ufumu wa Kumwamba uli wofanafana ndi chotupitsa mikate, chimene mkazi anachitenga, nachibisa m'miyeso itatu ya ufa, kufikira wonse unatupa.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa