Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Eksodo 10:20 - Buku Lopatulika

20 Koma Yehova analimbitsa mtima wa Farao, ndipo sanalole ana a Israele amuke.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

20 Koma Yehova analimbitsa mtima wa Farao, ndipo sanalole ana a Israele amuke.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

20 Koma Chauta adamuumitsabe mtima Farao, ndipo sadaŵalole Aisraele kuti apite.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

20 Koma Yehova anawumitsa mtima wa Farao, ndipo sanalole kuti Aisraeli apite.

Onani mutuwo Koperani




Eksodo 10:20
13 Mawu Ofanana  

Ndipo Yehova anati kwa Mose, Lowa kwa Farao; pakuti ndaumitsa mtima wake, ndi mtima wa anyamata ake, kuti ndiike zizindikiro zanga izi pakati pao;


Ndipo Yehova anabweza mphepo yolimbatu ya kumadzulo, imene inapita nalo dzombe niliponya mu Nyanja Yofiira: silinatsale dzombe limodzi pakati pa malire onse a Ejipito.


Koma Yehova analimbitsa mtima wake wa Farao, ndipo anakana kuwaleka amuke.


Ndipo Mose ndi Aroni anachita zozizwa izi zonse pamaso pa Farao; koma Yehova analimbitsa mtima wake wa Farao, ndipo sanalole ana a Israele atuluke m'dziko lake.


Koma Ine ndidziwa kuti mfumu ya Aejipito siidzalola inu kumuka, inde lingakhale ndi dzanja lamphamvu ai.


Ndipo Yehova ananena ndi Mose, Pakumuka iwe kubwerera kunka ku Ejipito, usamalire uchite zozizwa zonse ndaziika m'dzanja lako, pamaso pa Farao; koma Ine ndidzalimbitsa mtima wake kuti asadzalole anthu kupita.


Koma Yehova analimbitsa mtima wa Farao, kuti sanamvere iwo; monga Yehova adalankhula ndi Mose.


Chotero Iye achitira chifundo amene Iye afuna, ndipo amene Iye afuna amuumitsa mtima.


Koma Sihoni mfumu ya Hesiboni sanatilole kupitira kwao; popeza Yehova Mulungu wanu anaumitsa mzimu wake, nalimbitsa mtima wake, kuti ampereke m'dzanja lanu, monga lero lino.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa