Danieli 9:22 - Buku Lopatulika22 Ndipo anandilangiza ine, ndi kulankhula nane, nati, Daniele iwe, ndatuluka tsopano ine kukuzindikiritsa mwaluntha. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201422 Ndipo anandilangiza ine, ndi kulankhula nane, nati, Daniele iwe, ndatuluka tsopano ine kukuzindikiritsa mwaluntha. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero22 Anandilangiza kuti, “Danieli ndabwera tsopano kuti ndikupatse nzeru kuti uzitha kumvetsa zinthu. Onani mutuwo |