Danieli 8:23 - Buku Lopatulika23 Ndipo potsiriza pake pa ufumu wao, atakwanira olakwa, idzauka mfumu ya nkhope yaukali yakuzindikira zinsinsi. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201423 Ndipo potsiriza pake pa ufumu wao, atakwanira olakwa, idzauka mfumu ya nkhope yaukali yakuzindikira zinsinsi. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero23 “Pa masiku otsiriza a maufumuwa, machimo awo atachulukitsa, padzadzuka mfumu yaukali ndi yochenjera kwambiri. Onani mutuwo |