Danieli 8:21 - Buku Lopatulika21 Ndi tonde wamanyenje ndiye mfumu ya Agriki, ndi nyanga yaikulu ili pakati pamaso ake ndiyo mfumu yoyamba. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201421 Ndi tonde wamanyenje ndiye mfumu ya Agriki, ndi nyanga yaikulu ili pakati pa maso ake ndiyo mfumu yoyamba. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero21 Mbuzi yayimuna ija ndi mfumu ya Agriki, ndipo nyanga yayikulu pakati pa maso ake aja ndi mfumu yoyamba. Onani mutuwo |