Danieli 8:2 - Buku Lopatulika2 Ndipo ndinaona m'masomphenya; tsono kunali, pakuwaona ine ndinali mu Susa, m'nyumba ya mfumu, ndiwo m'dziko la Elamu; ndinaona m'masomphenya kuti ndinali kumtsinje Ulai. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Ndipo ndinaona m'masomphenya; tsono kunali, pakuwaona ine ndinali m'Susa, m'nyumba ya mfumu, ndiwo m'dziko la Elamu; ndinaona m'masomphenya kuti ndinali kumtsinje Ulai. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Ndinaona mʼmasomphenya kuti ndinali mu mzinda wotetezedwa wa Susa mʼchigawo cha Elamu. Mʼmasomphenyawo ndinaona nditayima pafupi ndi mtsinje wa Ulai. Onani mutuwo |