Danieli 7:15 - Buku Lopatulika15 Koma ine Daniele, mzimu wanga unalaswa m'kati mwa thupi langa, ndi masomphenya a m'mtima mwanga anandivuta. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201415 Koma ine Daniele, mzimu wanga unalaswa m'kati mwa thupi langa, ndi masomphenya a m'mtima mwanga anandivuta. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero15 “Ine Danieli ndinavutika mu mzimu, ndipo zimene ndinaziona mʼmasomphenya zinandisautsa mʼmaganizo. Onani mutuwo |