Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Danieli 5:24 - Buku Lopatulika

24 Pamenepo nsonga ya dzanja inatumidwa kuchokera pamaso pake, nililembedwa lembali.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

24 Pamenepo nsonga ya dzanja inatumidwa kuchokera pamaso pake, nililembedwa lembali.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

24 Choncho Iye watumiza dzanja limene lalemba mawu amenewa.

Onani mutuwo Koperani




Danieli 5:24
2 Mawu Ofanana  

Ndipo lemba lolembedwa ndi ili: MENE MENE TEKEL ndi PARSIN.


Nthawi yomweyo zinabuka zala za dzanja la munthu, ndipo zinalemba pandunji pa choikaponyali, pomata pa khoma la chinyumba cha mfumu; ndipo mfumu inaona nsonga yake ya dzanja lidalembalo.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa